NJIRA ZOTETEZERA ANA KUNKHAZA ZOGONANA NDI KU GWIRIRIDWA

NJIRA ZOTETEZERA ANA KUNKHAZA ZOGONANA NDI KU GWIRIRIDWA

M’chaka cha 2023 chinali ndizambiri zomvesa chisoni monga kungwa kwa mvula yaukali yomwe adapha anthu ambiri komaso tinamaliza ndi kuva nkhani ya abusa ena ku Mangochi omwe adapezeka wolakwa pa mlandu wongwirira mwana wake komaso tidava nkhani ya mtsikana wina amene adamphedwa mboma la Thyolo ndi azibambo ena amene adamungwiririra. 


Ife ngati bungu tikuthokoza mtsogolereri wanthu wakele bambo Maxwell Matewere amene walora kuti kuyambira mchaka chino cha 2024 tingawe mwaulele Buku lomwe adalemba lomphunzitsa anthu za njira zotetezera ana kunkhaza zogonana ndi ku ngwiriridwa.

 
ZA MKATI MWA BUKU 
Ana amakumana ndi nkhanza zosiyanasiyana zomwe zimabweretsa manzunzo aakulu komanso kuphedwa kumene pofuna kubisa umboni. Pachifukwa cha ichi, ife mbuyomu tinayambitsa ntchito zosiyanasiyana zomwe cholinga chake ndi kudziwitsa anthu za nkhanza zomwe ana amakumana nazo monga kuthetsa maukwati a ana, kuzembaitsidwa, kuchotsedwa ziwalo komanso kugwiritsidwa ntchito zoposa msinkhu wawo mwazina. 

“BETRAYAL OF TRUST” BOOK

BETRAYAL OF TRUST BOOK written by Maxwell Matewere provides a compelling look into the dark and inhuman side of child sexual abuse and invites each one of us to join the growing response against child sexual abuse affecting many innocent, defenceless, and vulnerable children in Malawi.


The Book inform the readers about the national laws that protect children from defilement and sexual abuse in Malawi, how parents can dictate and prevent such incidents before they happen, what type of treatment Victim needs, about HIV postexposure prophylaxis and about the punishment given to offenders.